Numeri 1:39 - Buku Lopatulika39 owerengedwa ao a fuko la Dani, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201439 owerengedwa ao a fuko la Dani, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa39 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Dani, adapezeka kuti ali 62,700. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero39 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Dani chinali 62,700. Onani mutuwo |