Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:39 - Buku Lopatulika

39 owerengedwa ao a fuko la Dani, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

39 owerengedwa ao a fuko la Dani, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

39 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Dani, adapezeka kuti ali 62,700.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

39 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Dani chinali 62,700.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:39
4 Mawu Ofanana  

A ana a Dani, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


A ana a Asere, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu ziwiri kudza mazana asanu ndi awiri.


Mabanja onse a Asuhamu monga mwa owerengedwa ao ndiwo zikwi makumi asanu ndi limodzi mphambu zinai kudza mazana anai.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa