Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Numeri 1:25 - Buku Lopatulika

25 owerengedwa ao a fuko la Gadi, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

25 owerengedwa ao a fuko la Gadi, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

25 Tsono ataŵerenga maina onse a m'fuko la Gadi, adapezeka kuti ali 45,650.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

25 Chiwerengero cha anthu ochokera mʼfuko la Gadi chinali 45, 650.

Onani mutuwo Koperani




Numeri 1:25
4 Mawu Ofanana  

A ana a Gadi, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


A ana a Yuda, kubadwa kwao, monga mwa mabanja ao, monga mwa nyumba za makolo ao, powerenga maina, kuyambira a zaka makumi awiri ndi mphambu, onse akutulukira kunkhondo;


Ndi khamu lake, ndi owerengedwa ake, ndiwo zikwi makumi anai mphambu zisanu kudza mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu.


Iwo ndiwo mabanja a ana a Gadi, monga mwa owerengedwa ao, zikwi makumi anai ndi mazana asanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa