Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:62 - Buku Lopatulika

62 ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

62 ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi anai kudza awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

62 A banja la Delaya, a banja la Tobiya, a banja la Nekoda 642.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

62 Zidzukulu za Delaya, zidzukulu za Tobiya ndi zidzukulu za Nekoda 642.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:62
3 Mawu Ofanana  

ana a Delaya, ana a Tobiya, ana a Nekoda, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


Ndipo okwera kuchokera ku Telemela, Teleharisa, Kerubi, Adoni, ndi Imeri, ndi awa; koma sanakhoze kutchula nyumba za makolo ao, kapena mbumba zao, ngati ali a Israele;


Ndi a ansembe: ana a Hobaya, ana a Hakozi, ana a Barizilai, amene anadzitengera mkazi wa ana aakazi a Barizilai Mgiliyadi, natchedwa ndi dzina lao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa