Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:41 - Buku Lopatulika

41 Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

41 Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

41 A banja la Pasuri 1,247.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

41 Zidzukulu za Pasi-Huri 1,247

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:41
6 Mawu Ofanana  

wachisanu Malikiya, wachisanu ndi chimodzi Miyamini,


ndi Adaya mwana wa Yerohamu, mwana wa Pasuri, mwana wa Malikiya, ndi Maasai mwana wa Adiyele, mwana wa Yazera, mwana wa Mesulamu, mwana wa Mesilemiti, mwana wa Imeri,


Ndi a ana a Pasuri: Eliyoenai, Maaseiya, Ismaele, Netanele, Yozabadi, ndi Elasa.


Ana a Pasuri, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi anai ndi asanu ndi awiri.


Ana a Imeri, chikwi chimodzi mphambu makumi asanu kudza awiri.


Ana a Harimu, chikwi chimodzi mphambu khumi limodzi kudza asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa