Nehemiya 7:4 - Buku Lopatulika4 Mzindawo tsono ndi wachitando, ndi waukulu; koma anthu anali m'mwemo ngowerengeka, nyumba zomwe sizinamangike. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Mudziwo tsono ndi wachitando, ndi waukulu; koma anthu anali m'mwemo ngowerengeka, nyumba zomwe sizinamangike. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu, koma anthu okhala mumzindamo anali oŵerengeka, ndipo munalibe nyumba zambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Tsono mzinda wa Yerusalemu unali wotambasuka ndiponso waukulu koma munali anthu ochepa ndipo nyumba zinali zisanamangidwe. Onani mutuwo |