Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:31 - Buku Lopatulika

31 Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

31 Amuna a ku Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

31 Amuna a ku Mikimasi 122.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

31 Anthu a ku Mikimasi 122

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:31
6 Mawu Ofanana  

Anthu a Mikimasi, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza awiri.


Amuna a ku Rama ndi Geba, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza mmodzi.


Amuna a ku Betele ndi Ai, zana limodzi mphambu makumi awiri kudza atatu.


Wafika ku Ayati, wapitirira kunka ku Migironi; pa Mikimasi asunga akatundu ake;


Ndipo a ku kaboma ka Afilisti anatuluka kunja ku mpata wa ku Mikimasi.


Ndipo Afilisti anasonkhana kuti akamenyane ndi Aisraele, anali nao magaleta zikwi makumi atatu, ndi apakavalo zikwi zisanu ndi chimodzi, ndi anthu akuchuluka monga mchenga wa m'mphepete mwa nyanja. Iwowa anakwera namanga zithando ku Mikimasi kum'mawa kwa Betaveni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa