Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:18 - Buku Lopatulika

18 Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi, kudza asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

18 Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi, kudza asanu ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

18 A banja la Adonikamu 667.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

18 Zidzukulu za Adonikamu 667

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:18
3 Mawu Ofanana  

Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi mmodzi.


Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.


Ana a Bigivai, zikwi ziwiri mphambu makumi asanu ndi limodzi kudza asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa