Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 7:17 - Buku Lopatulika

17 Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

17 Ana a Azigadi, zikwi ziwiri mphambu mazana atatu kudza makumi awiri ndi awiri.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

17 A banja la Azigadi 2,322.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

17 Zidzukulu za Azigadi 2,322

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 7:17
3 Mawu Ofanana  

Ana a Azigadi, chikwi chimodzi mphambu mazana awiri kudza makumi awiri ndi awiri.


Ana a Bebai, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi awiri kudza asanu ndi atatu.


Ana a Adonikamu, mazana asanu ndi limodzi mphambu makumi asanu ndi limodzi, kudza asanu ndi awiri.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa