Nehemiya 5:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo pakumva kulira kwao, ndi mau ao, kunandiipira kwambiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo pakumva kulira kwao, ndi mau ao, kunandiipira kwambiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Ine nditamva madandaulo amenewo, ndidapsa mtima kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Nditamva madandawulo awo ndi zimene amanenazi ndinapsa mtima kwambiri. Onani mutuwo |