Nehemiya 4:17 - Buku Lopatulika17 Iwo omanga linga, ndi iwo osenza katundu, posenza, anachita aliyense ndi dzanja lake lina logwira ntchito, ndi lina logwira chida; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Iwo omanga linga, ndi iwo osenza katundu, posenza, anachita aliyense ndi dzanja lake lina logwira ntchito, ndi lina logwira chida; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Anthu onyamula zinyalala aja ankagwira ntchito ndi dzanja limodzi, kwinaku atagwira chida chankhondo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 amene ankamanga khoma. Anthu onyamula zinyalala aja ankagwira ntchito ndi dzanja limodzi, dzanja linali atanyamula chida chankhondo. Onani mutuwo |