Nehemiya 4:12 - Buku Lopatulika12 Ndipo kunali, atafika Ayuda okhala pafupi pao ochokera pamalo ponse, anatiuza ife kakhumi, Bwererani kwa ife. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndipo kunali, atafika Ayuda okhala pafupi pao ochokera pamalo ponse, anatiuza ife kakhumi, Bwererani kwa ife. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Tsono Ayuda okhala pafupi ndi adani athuwo ankabwera natichenjeza kakhumi konse kuti “Iwo aja adzafika kudzalimbana nanu kuchokera kulikonse kumene amakhala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ndipo Ayuda amene ankhala pafupi ndi adani athuwo anabwera kakhumi konse kuchokera konse kumene ankakhala kudzatiwuza kuti tibwereko ku ntchito. Onani mutuwo |