Nehemiya 4:11 - Buku Lopatulika11 Nati adani athu, Sadzadziwa kapena kuona mpaka talowa pakati pao, ndi kuwapha, ndi kuleketsa ntchitoyi. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Nati adani athu, Sadzadziwa kapena kuona mpaka talowa pakati pao, ndi kuwapha, ndi kuleketsa ntchitoyi. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Adani athu ankanena zakuti ife Ayuda sitidzadziŵa kapena kuwona kanthu, mpaka iwo atafika pakati pathu, natipha ndi kuletsa ntchito yathuyi. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Adani athunso anati, “Iwo asanadziwe izi, kapena kutiona, tidzakhala tili pakati pawo ndipo tidzawapha ndi kuyimitsa ntchitoyo.” Onani mutuwo |