Nehemiya 3:5 - Buku Lopatulika5 Ndi pambali pao anakonza Atekowa; koma omveka ao sanapereke makosi ao kuntchito ya Mbuye wao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndi pambali pao anakonza Atekowa; koma omveka ao sanapereke makosi ao kuntchito ya Mbuye wao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Pambali pa iwowo Atekowa adakonza chigawo china, koma atsogoleri ao adakana kugwira ntchito imene akuluakulu ao adaŵapatsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Pambali pa iwowa anthu a ku Tekowa anakonza chigawo china. Koma wolemekezeka awo anakana kugwira ntchito imene akuluakulu awo anawapatsa. Onani mutuwo |