Nehemiya 2:4 - Buku Lopatulika4 Ndipo mfumu inati kwa ine, Ufunanji iwe? Pamenepo ndinapemphera Mulungu wa Kumwamba. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Ndipo mfumu inati kwa ine, Ufunanji iwe? Pamenepo ndinapemphera Mulungu wa Kumwamba. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Tsono mfumu idandifunsa kuti, “Tsono umati undipemphe chiyani?” Pamenepo ndidapemphera kwa Mulungu Wakumwamba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Apo mfumu inandifunsa kuti, “Tsono ukufuna kundipempha chiyani?” Ndipo ine ndinapemphera kwa Mulungu Wakumwamba. Onani mutuwo |