Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 2:11 - Buku Lopatulika

11 Motero ndinafika ku Yerusalemu, ndi kukhalako masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Motero ndinafika ku Yerusalemu, ndi kukhalako masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Choncho ndidafika ku Yerusalemu ndipo ndidakhala kumeneko masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ndinafika ku Yerusalemu, ndipo ndinakhala kumeneko masiku atatu.

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 2:11
2 Mawu Ofanana  

Ndipo tinafika ku Yerusalemu ndi kukhalako masiku atatu.


Ndipo ndinauka usiku, ine ndi amuna owerengeka nane, osauza munthu yense ine choika Mulungu wanga m'mtima mwanga ndichitire Yerusalemu; panalibenso nyama ina nane, koma nyama imene ndinakhalapo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa