Nehemiya 13:23 - Buku Lopatulika23 Masiku aja ndinaonanso Ayudawo anadzitengera akazi a Asidodi, Aamoni, ndi Amowabu, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Masiku aja ndinaonanso Ayudawo anadzitengera akazi a Asidodi, Aamoni, ndi Amowabu, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Nthaŵi imeneyo ndidaona Ayuda amene adaakwatira akazi a ku Asidodi, a ku Amoni ndiponso a ku Mowabu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Masiku amenewo ndinaonanso anthu a ku Yuda amene anakwatira akazi ochokera ku Asidodi, Amoni ndi Mowabu. Onani mutuwo |