Nehemiya 13:20 - Buku Lopatulika20 Momwemo eni malonda ndi ogulitsa malonda ali onse, anagona kunja kwa Yerusalemu kamodzi kapena kawiri. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201420 Momwemo eni malonda ndi ogulitsa malonda ali onse, anagona kunja kwa Yerusalemu kamodzi kapena kawiri. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa20 Motero anthu amalonda ogulitsa zinthu zamitundumitundu ankagona kunja kwa mzinda wa Yerusalemu kamodzi kapena kaŵiri konse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero20 Choncho kamodzi kapena kawiri anthu amalonda ndi anthu ogulitsa katundu osiyanasiyana ankagona usiku wonse kunja kwa Yerusalemu. Onani mutuwo |