Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 12:32 - Buku Lopatulika

32 ndi pambuyo pao anayenda Hosaya, ndi limodzi la magawo awiri a akulu a Yuda,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

32 ndi pambuyo pao anayenda Hosaya, ndi limodzi la magawo awiri a akulu a Yuda,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

32 Pambuyo pao pankadza Hosaya ndi theka la akuluakulu aja,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

32 Pambuyo pawo panali Hosayia, theka la atsogoleri a Yuda aja

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 12:32
2 Mawu Ofanana  

Pamenepo ndinakwera nao akulu a Yuda pa lingali, ndinaikanso oyamikira magulu awiri akulu oyenda molongosoka; lina loyenda ku dzanja lamanja palinga kunka ku Chipata cha Kudzala;


ndi Azariya, Ezara ndi Mesulamu,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa