Nehemiya 11:25 - Buku Lopatulika25 Ndi ana ena a Yuda anakhala m'midzi ya kuminda yao, mu Kiriyati-Ariba ndi midzi yake, ndi mu Diboni ndi midzi yake, ndi mu Yekabizeele ndi midzi yake, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201425 Ndi ana ena a Yuda anakhala m'midzi ya kuminda yao, m'Kiriyati-Ariba ndi milaga yake, ndi m'Diboni ndi milaga yake, ndi m'Yekabizeele ndi midzi yake, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa25 Anthu ena a fuko la Yuda ankakhala ku Kiriyati-Ariba ndi midzi yake, ku Diboni ndi midzi yake, ku Yekabizeele ndi midzi yake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero25 Anthu ena a fuko la Yuda ankakhala ku Kiriyati-Ariba ndi midzi yake, ku Diboni ndi midzi yake, ku Yekabizeeli ndi midzi yake, Onani mutuwo |