Nehemiya 11:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo anthu anadalitsa amuna onse akudzinenera mwaufulu kuti adzakhala mu Yerusalemu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo anthu anadalitsa amuna onse akudzinenera mwaufulu kuti adzakhala m'Yerusalemu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Ndipo anthu adayamika anzao onse amene adadzipereka kuti azikhala ku Yerusalemu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Anthu anayamikira onse amene anadzipereka kuti azikhala mu Yerusalemu. Onani mutuwo |