Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Nehemiya 10:10 - Buku Lopatulika

10 ndi abale ao: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

10 ndi abale ao: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

10 ndi abale ao aŵa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

10 ndi abale awo awa: Sebaniya, Hodiya, Kelita, Pelaya, Hanani,

Onani mutuwo Koperani




Nehemiya 10:10
10 Mawu Ofanana  

Ndi ana a mkazi wa Hodiya, mlongo wake wa Nahamu, ndiwo atate a Keila Mgarimi ndi Esitemowa Mmaaka.


Ndi a Alevi: Yozabadi, ndi Simei, ndi Kelaya (ndiye Kelita), Petahiya, Yuda, ndi Eliyezere.


Ndipo pa tsiku lachinai siliva ndi golide ndi zipangizo zinayesedwa m'nyumba ya Mulungu wathu, m'dzanja la Meremoti mwana wa Uriya wansembe, ndi pamodzi naye Eleazara mwana wa Finehasi, ndi pamodzi nao Yozabadi mwana wa Yesuwa, ndi Nowadiya mwana wa Binuyi, Alevi;


Mika, Rehobu, Hasabiya,


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa mwana wa Azaniya, Binuyi wa ana a Henadadi, Kadimiyele;


Ndi Alevi ndiwo Yesuwa, Binuyi, Kadimiyele, Serebiya, Yuda, ndi Mataniya; iye ndi abale ake amatsogolera mayamiko.


Potsatizana naye Binuyi mwana wa Henadadi anakonza gawo lina, kuyambira kunyumba ya Azariya kufikira popindirira kufikira kungodya.


A Levi: ana a Yesuwa, a Kadimiyele, a ana a Hodeva, makumi asanu ndi awiri kudza anai.


Ndi Yesuwa, ndi Bani, ndi Serebiya, Yamini, Akubu, Sabetai, Hodiya, Maaseiya, Kelita, Azariya, Yozabadi, Hanani, Pelaya, ndi Alevi, anadziwitsa anthu chilamulocho; ndi anthu anali chilili pamalo pao.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa