Mlaliki 9:7 - Buku Lopatulika7 Tiye, idya zakudya zako mokondwa, numwe vinyo wako mosekera mtima; pakuti Mulungu wavomerezeratu zochita zako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Tiye, idya zakudya zako mokondwa, numwe vinyo wako mosekera mtima; pakuti Mulungu wavomerezeratu zochita zako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Ndiye iwe usaope, uzidya chakudya chako mokondwa, uzimwa vinyo wako ndi mtima wosangalala, pakuti Mulungu wavomereza kale zochita zakozo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Pita, kadye chakudya chako mokondwera ndi kumwa vinyo wako ndi mtima wosangalala, pakuti tsopano Mulungu akukondwera ndi zochita zako. Onani mutuwo |