Mlaliki 7:16 - Buku Lopatulika16 Usapambanitse kukhala wolungama; usakhale wanzeru koposa; bwanji ufuna kudziononga wekha? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Usapambanitse kukhala wolungama; usakhale wanzeru koposa; bwanji ufuna kudziononga wekha? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Ndiye usachite kunkitsa nako kulungama, kapena kunkitsa nazo nzeru. Nanga ufere ziti? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Usakhale wolungama kwambiri kapena wanzeru kwambiri, udziwonongerenji wekha? Onani mutuwo |