Mlaliki 5:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti monga mu unyinji wa maloto muli zachabe motero mochuluka mau; koma dziopa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti monga mu unyinji wa maloto muli zachabe motero mochuluka mau; koma dziopa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Maloto akachuluka pamachulukanso zokamba zachabechabe. Koma iwe uzilemekeza Mulungu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Maloto ochuluka ndi mawu ochuluka ndi zinthu zopandapake. Kotero lemekeza Mulungu. Onani mutuwo |