Mlaliki 5:16 - Buku Lopatulika16 Ichinso ndi choipa chowawa, chakuti adzangopita monse monga anadza; ndipo wodzisautsa chabe adzaona phindu lanji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ichinso ndi choipa chowawa, chakuti adzangopita monse monga anadza; ndipo wodzisautsa chabe adzaona phindu lanji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Chimenechinso nchoipa chomvetsa chisoni kwambiri: kuti munthu adzapita monga momwe adabwerera. Nanga phindu lake nchiyani, popeza kuti iyeyo adagwira pachabe ntchito yolemetsa? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Izinso ndi zoyipa kwambiri: munthu adzapita monga momwe anabwerera, ndipo iye amapindula chiyani, pakuti amagwira ntchito yolemetsa yopanda phindu? Onani mutuwo |