Mlaliki 5:17 - Buku Lopatulika17 Inde masiku ake onse amadya mumdima, ndipo zimchulukira chisoni ndi nthenda ndi mkwiyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Inde masiku ake onse amadya mumdima, nizimchulukira chisoni ndi nthenda ndi mkwiyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Masiku ake onse moyo wake unali wodzaza ndi mdima ndi chisoni, unali moyo wa mavuto, matenda ndi nkhaŵa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Masiku ake onse ndi odzaza ndi mdima, kukhumudwa kwakukulu, masautso ndi nkhawa. Onani mutuwo |
Ndipo inanena naye, Munthu anakwera kukomana nafe, nati kwa ife, Kabwerereni kwa mfumu imene inakutumani inu, nimunene nayo, Atero Yehova, Kodi ndi popeza palibe Mulungu mwa Israele, kuti ulikutuma kukafunsira kwa Baala-Zebubi mulungu wa ku Ekeroni? Chifukwa chake sudzatsika pakama pamene wakwerapo, koma udzafa ndithu.