Mlaliki 3:12 - Buku Lopatulika12 Ndidziwa kuti iwo alibe ubwino, koma kukondwa ndi kuchita zabwino pokhala ndi moyo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Ndidziwa kuti iwo alibe ubwino, koma kukondwa ndi kuchita zabwino pokhala ndi moyo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ndikudziŵa kuti kwa anthu palibe chabwino china choposa kukhala osangalala ndi kumadzikondweretsa nthaŵi yonse ya moyo wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ine ndikudziwa kuti palibenso kanthu kabwino kwa anthu kopambana kusangalala ndi kuchita zabwino pamene ali ndi moyo. Onani mutuwo |