Mlaliki 3:13 - Buku Lopatulika13 Ndiponso kuti munthu yense adye namwe naone zabwino m'ntchito zake zonse; ndiwo mtulo wa Mulungu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Ndiponso kuti munthu yense adye namwe naone zabwino m'ntchito zake zonse; ndiwo mtulo wa Mulungu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndi mphatso ya Mulungu kwa anthu kuti azidya, azimwa ndi kumakondwera ntchito zao zolemetsa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndi mphatso ya Mulungu kwa munthu kuti azidya, azimwa ndi kumakondwera ndi ntchito zake zolemetsa. Onani mutuwo |