Mlaliki 3:1 - Buku Lopatulika1 Kanthu kalikonse kali ndi nthawi yake ndi chofuna chilichonse cha pansi pa thambo chili ndi mphindi yake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Kanthu kalikonse kali ndi nthawi yake ndi chofuna chilichonse cha pansi pa thambo chili ndi mphindi yake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pansi pano chinthu chilichonse chili ndi nyengo yake ndi nthaŵi yake yomwe adaika Mulungu: Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Chinthu chilichonse chili ndi nthawi yake, ndi nyengo yake yomwe anayika Mulungu: Onani mutuwo |