Mlaliki 2:23 - Buku Lopatulika23 Pakuti masiku ake onse ndi zisoni, vuto lake ndi kumliritsa; ngakhale usiku mtima wake supuma. Ichinso ndi chabe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 Pakuti masiku ake onse ndi zisoni, vuto lake ndi kumliritsa; ngakhale usiku mtima wake supuma. Ichinso ndi chabe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Masiku ake onse amakhala achisoni, ntchito yake imakhala yovuta. Ndi usiku womwe mtima wake supumula. Zimenezinso nzopanda phindu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Masiku ake onse amakhala achisoni, ntchito yake imakhala yovuta; ngakhale usiku womwe, mtima wake supumula. Izinso ndi zopandapake. Onani mutuwo |