Mlaliki 2:22 - Buku Lopatulika22 Pakuti munthu ali ndi chiyani m'ntchito zake zonse, ndi m'kusauka kwa mtima wake amasauka nazozo kunja kuno? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Pakuti munthu ali ndi chiyani m'ntchito zake zonse, ndi m'kusauka kwa mtima wake amasauka nazozo kunja kuno? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Kodi munthu amapindulanji pa ntchito zonse zolemetsa ndi zodetsa nkhaŵa zimene amazichita pansi pano? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Kodi munthu amapindulanji pa ntchito zonse zolemetsa ndi zodetsa nkhawa zimene amazichita pansi pano? Onani mutuwo |