Mlaliki 2:13 - Buku Lopatulika13 Pamenepo ndinazindikira kuti nzeru ipambana utsiru kwambiri, monga kuunika kupambana mdima. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Pamenepo ndinazindikira kuti nzeru ipambana utsiru kwambiri, monga kuunika kupambana mdima. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Ndidaona kuti inde nzeru nzopambana uchitsiru, monga momwe kuŵala kumapambanira mdima. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Ndinaona kuti nzeru ndi yopambana uchitsiru, monga momwe kuwala kumapambanira mdima. Onani mutuwo |