Mlaliki 12:2 - Buku Lopatulika2 ngakhale lisanade dzuwa, ndi kuunika, ndi mwezi, ndi nyenyezi, mitambo ndi kubweranso italeka mvula; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 ngakhale lisanade dzuwa, ndi kuunika, ndi mwezi, ndi nyenyezi, mitambo ndi kubweranso italeka mvula; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Nthaŵi ya ukalamba wako, dzuŵa, kuŵala, mwezi, nyenyezi, zonse zidzakudera, ndipo mitambo idzabweranso mvula itagwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Nthawi ya ukalamba wako, dzuwa ndi kuwala, mwezi ndi nyenyezi zidzada. Mitambo idzabweranso mvula itagwa. Onani mutuwo |