Mlaliki 1:18 - Buku Lopatulika18 Pakuti m'nzeru yambiri muli chisoni chambiri; ndi yemwe aenjezera chidziwitso aenjezera zowawa. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201418 Pakuti m'nzeru yambiri muli chisoni chambiri; ndi yemwe aenjezera chidziwitso aenjezera zowawa. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa18 Paja nzeru zambiri zimadzetsa chisoni chambiri, munthu akamaonjezera nzeru, ndiye kuti akuwonjezeranso chisoni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero18 Pakuti nzeru zochuluka zimabweretsa chisoni chochulukanso: chidziwitso chochuluka, zowawa zochulukanso. Onani mutuwo |