Mika 6:5 - Buku Lopatulika5 Anthu anga, kumbukiranitu chofunsira Balaki mfumu ya Mowabu, ndi chomuyankha Balamu mwana wa Beori, kuyambira ku Sitimu kufikira ku Giligala; kuti mudziwe zolungama za Yehova. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Anthu anga, kumbukiranitu chofunsira Balaki mfumu ya Mowabu, ndi chomuyankha Balamu mwana wa Beori, kuyambira ku Sitimu kufikira ku Giligala; kuti mudziwe zolungama za Yehova. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Inu anthu anga, kumbukirani zimene Balaki, mfumu ya ku Mowabu, adaafuna kukuchitani, ndiponso m'mene Balamu mwana wa Beori adamuyankhira. Kumbukirani zimene zidachitika pa ulendo wochoka ku Sitimu kupita ku Giligala. Kumbukirani zonsezi kuti muzindikire zimene Ine Chauta ndidachita pofuna kukupulumutsani.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Anthu anga, kumbukirani zimene Balaki mfumu ya ku Mowabu inafuna kukuchitirani ndiponso zimene Balaamu mwana wa Beori anayankha. Kumbukirani zomwe zinachitika pa ulendo wochoka ku Sitimu kupita ku Giligala, kuti mudziwe machitidwe olungama a Yehova.” Onani mutuwo |