Mika 3:7 - Buku Lopatulika7 Ndipo alauli adzachita manyazi, ndi olosa adzathedwa nzeru; ndipo onsewo adzasunama; pakuti kuyankha kwa Mulungu kulibe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Ndipo alauli adzachita manyazi, ndi olosa adzathedwa nzeru; ndipo onsewo adzasunama; pakuti kuyankha kwa Mulungu kulibe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Alauli adzaŵanyazitsa, oombeza maula adzaŵachititsa manyazi. Onse adzangoti pakamwa gwirire, chifukwa Mulungu sakuŵayankha. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Alosi adzachita manyazi ndipo owombeza mawula adzanyazitsidwa. Onse adzaphimba nkhope zawo chifukwa Mulungu sakuwayankha.” Onani mutuwo |
Ndipo Samuele ananena ndi Saulo, Wandivutiranji kundikweretsa kuno? Saulo nayankha, Ndilikusautsika kwambiri, pakuti Afilisti aponyana nkhondo ndi ine, ndipo Mulungu anandichokera, osandiyankhanso, kapena ndi aneneri, kapena ndi maloto; chifukwa chake ndakuitanani, kuti mundidziwitse chimene ndiyenera kuchita.