Mika 3:2 - Buku Lopatulika2 Inu amene mudana nacho chokoma ndi kukondana nacho choipa; inu akumyula khungu lao pathupi pao, ndi mnofu wao pa mafupa ao; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Inu amene mudana nacho chokoma ndi kukondana nacho choipa; inu akumyula khungu lao pathupi pao, ndi mnofu wao pa mafupa ao; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Mumadana ndi zabwino, mumakonda zoipa. Anthu anga mumaŵasenda amoyo, ndi kukangadzula mnofu wao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 inu amene mumadana ndi zabwino ndi kukonda zoyipa; inu amene mumasenda khungu la anthu anga, ndipo mumakungunula mnofu pa mafupa awo; Onani mutuwo |