Mika 3:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo ndinati, Imvanitu, inu akulu a Yakobo, ndi oweruza a nyumba ya Israele; simuyenera kodi kudziwa chiweruzo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo ndinati, Imvanitu, inu akulu a Yakobo, ndi oweruza a nyumba ya Israele; simuyenera kodi kudziwa chiweruzo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Ine ndidati, “Imvani inu akuluakulu a Yakobe, olamulira a banja la Israele! Kodi oyenera kudziŵa chilungamo sindinu? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Ndipo ine ndinati, “Tamverani, inu atsogoleri a Yakobo, inu olamulira nyumba ya Israeli. Kodi sindinu oyenera kudziwa kuweruza molungama, Onani mutuwo |