Mateyu 9:5 - Buku Lopatulika5 Pakuti chapafupi nchiti, kunena, Machimo ako akhululukidwa; kapena kunena, Tanyamuka. Nuyende? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Pakuti chapafupi nchiti, kunena, Machimo ako akhululukidwa; kapena kunena, Tanyamuka. Nuyende? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Chapafupi koposa nchiti, kunena kuti, ‘Machimo ako akhululukidwa,’ kapena kunena kuti, ‘Dzuka, yamba kuyenda?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Chapafupi ndi chiti kunena kuti, ‘Machimo ako akhululukidwa’ kapena kunena kuti, ‘Imirira ndipo yenda?’ Onani mutuwo |