Mateyu 9:34 - Buku Lopatulika34 Koma Afarisi analinkunena, Atulutsa ziwanda ndi mphamvu zake za mfumu ya ziwanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201434 Koma Afarisi analinkunena, Atulutsa ziwanda ndi mphamvu zake za mfumu ya ziwanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa34 Koma Afarisi adati, “Ameneyu amatulutsa mizimu yoipa ndi mphamvu zomupatsa mfumu ya mizimu yoipa ija.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero34 Koma Afarisi anati, “Akutulutsa mizimu yoyipa ndi mphamvu ya mkulu wa ziwanda.” Onani mutuwo |