Mateyu 9:32 - Buku Lopatulika32 Ndipo pamene iwo analikutuluka, onani, anabwera naye kwa Iye munthu wosalankhula, wogwidwa ndi chiwanda. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201432 Ndipo pamene iwo analikutuluka, onani, anabwera naye kwa Iye munthu wosalankhula, wogwidwa ndi chiwanda. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa32 Pamene iwowo ankatuluka m'nyumbamo, anthu ena adabwera kwa Yesu ndi munthu wosatha kulankhula, chifukwa chogwidwa ndi mzimu woipa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero32 Pamene iwo ankatuluka kunja, anthu anabwera kwa Iye ndi munthu wogwidwa ndi mzimu wosayankhula. Onani mutuwo |