Mateyu 9:3 - Buku Lopatulika3 Ndipo onani, ena a alembi ananena mumtima mwao, Uyu achitira Mulungu mwano. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Ndipo onani, ena a alembi ananena mumtima mwao, Uyu achitira Mulungu mwano. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Apo aphunzitsi ena a Malamulo adayamba kudzifunsa mumtima mwao kuti, “Munthu ameneyu akuchita chipongwe Mulungu.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Pamenepo aphunzitsi ena amalamulo anaganiza mu mtima mwawo kuti, “Munthu uyu akuchitira Mulungu mwano.” Onani mutuwo |