Mateyu 9:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo Yesu ananyamuka namtsata iye, ndi ophunzira ake omwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo Yesu ananyamuka namtsata iye, ndi ophunzira ake omwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Pamenepo Yesu adanyamuka, namtsatira pamodzi ndi ophunzira ake. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Yesu ndi ophunzira ake ananyamuka napita naye pamodzi. Onani mutuwo |