Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 9:19 - Buku Lopatulika

19 Ndipo Yesu ananyamuka namtsata iye, ndi ophunzira ake omwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

19 Ndipo Yesu ananyamuka namtsata iye, ndi ophunzira ake omwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

19 Pamenepo Yesu adanyamuka, namtsatira pamodzi ndi ophunzira ake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

19 Yesu ndi ophunzira ake ananyamuka napita naye pamodzi.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 9:19
6 Mawu Ofanana  

Ndipo Yesu ananena naye, Ndifika Ine, ndidzamchiritsa iye.


M'mene Iye analikulankhula nao zinthu zimenezo, onani, anadza munthu mkulu, namgwadira Iye, nanena, Wamwalira tsopanoli mwana wanga wamkazi, komatu mudze muike dzanja lanu pa iye, ndipo adzakhala ndi moyo.


Ndipo onani, mkazi, anali ndi nthenda yachidwalire zaka khumi ndi ziwiri, anadza pambuyo pake, nakhudza mphonje ya chofunda chake;


Yesu ananena nao, Chakudya changa ndicho kuti ndichite chifuniro cha Iye amene anandituma Ine, ndi kutsiriza ntchito yake.


za Yesu wa ku Nazarete, kuti Mulungu anamdzoza Iye ndi Mzimu Woyera ndi mphamvu; amene anapitapita nachita zabwino, nachiritsa onse osautsidwa ndi mdierekezi, pakuti Mulungu anali pamodzi ndi Iye.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa