Mateyu 9:1 - Buku Lopatulika1 Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumzinda kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumudzi kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Yesu adaloŵa m'chombo naoloka nyanja, nkukafika ku mzinda wakwao. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yesu analowa mʼbwato nawoloka, ndipo anabwera ku mudzi wa kwawo. Onani mutuwo |