Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 9:1 - Buku Lopatulika

1 Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumzinda kwao.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Ndipo Iye analowa m'ngalawa, naoloka, nadza kumudzi kwao.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Yesu adaloŵa m'chombo naoloka nyanja, nkukafika ku mzinda wakwao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Yesu analowa mʼbwato nawoloka, ndipo anabwera ku mudzi wa kwawo.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 9:1
8 Mawu Ofanana  

ndipo anachoka ku Nazarete nadza nakhalitsa Iye mu Kapernao wa pambali pa nyanja, m'malire a Zebuloni ndi Nafutali:


Musamapatsa chopatulikacho kwa agalu, ndipo musamaponya ngale zanu patsogolo pa nkhumba, kuti zingazipondereze ndi mapazi ao, ndi potembenuka zingang'ambe inu.


Ndipo Yesu, poona makamu ambiri a anthu akumzungulira Iye, analamulira ophunzira amuke kutsidya lina.


Ndipo pamene Iye atalowa m'ngalawa, ophunzira ake anamtsata Iye.


Ndipo pamene Yesu anaolokanso mungalawa tsidya lina, khamu lalikulu linasonkhana kwa Iye; ndipo Iye anali pambali pa nyanja.


Ndipo anthu aunyinji onse a dziko la Agerasa loyandikira anamfunsa Iye achoke kwa iwo; chifukwa anagwidwa ndi mantha aakulu. Ndipo Iye analowa m'ngalawa, nabwerera.


Ndipo pakubwera Yesu, khamu la anthu linamlandira Iye; pakuti onse analikumlindira Iye.


Iye wakukhala wosalungama achitebe zosalungama; ndi munthu wonyansa akhalebe wonyansa; ndi iye wakukhala wolungama achitebe cholungama; ndi iye amene ali woyera akhalebe woyeretsedwa.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa