Mateyu 8:2 - Buku Lopatulika2 Ndipo onani, wakhate anadza namgwadira Iye, nanena, Ambuye ngati mufuna mungathe kundikonza. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Ndipo onani, wakhate anadza namgwadira Iye, nanena, Ambuye ngati mufuna mungathe kundikonza. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Tsono munthu wina wakhate adadzamugwadira nati, “Ambuye, mutafuna mungathe kundichiritsa.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Ndipo munthu wakhate anadza kwa Yesu namugwadira nati, “Ambuye, ngati mufuna, mukhoza kundiyeretsa.” Onani mutuwo |