Mateyu 8:19 - Buku Lopatulika19 Ndipo anadza munthu mlembi, nati kwa Iye, Mphunzitsi, ndidzakutsatani Inu kulikonse mumukako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201419 Ndipo anadza munthu mlembi, nati kwa Iye, Mphunzitsi, ndidzakutsatani Inu kulikonse mumukako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa19 Koma nthaŵi yomweyo padafika mphunzitsi wina wa Malamulo namuuza kuti, “Aphunzitsi, ndizikutsatani kulikonse kumene muzipita.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero19 Ndipo mphunzitsi wa malamulo anabwera kwa Iye nati, “Aphunzitsi, ine ndidzakutsatani kulikonse kumene muzipita.” Onani mutuwo |