Mateyu 8:14 - Buku Lopatulika14 Ndipo pofika Yesu kunyumba ya Petro, anaona mpongozi wake ali gone, alikudwala malungo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201414 Ndipo pofika Yesu kunyumba ya Petro, anaona mpongozi wake ali gone, alikudwala malungo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa14 Pamene Yesu adakaloŵa m'nyumba ya Petro, adaona apongozi a Petro ali gone, akudwala malungo. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero14 Ndipo Yesu atalowa mʼnyumba ya Petro, anaona mpongozi wake wa Petro ali gone akudwala malungo. Onani mutuwo |