Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 7:20 - Buku Lopatulika

20 Inde chomwecho pa zipatso zao mudzawazindikira iwo.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

20 Inde chomwecho pa zipatso zao mudzawazindikira iwo.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

20 Choncho mudzaŵadziŵira zochita zao.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

20 Momwemonso, ndi zipatso zawo iwo mudzawazindikira.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 7:20
5 Mawu Ofanana  

Ukakoma mtengo, chipatso chake chomwe chikoma; ukaipa mtengo, chipatso chake chomwe chiipa; pakuti ndi chipatso chake mtengo udziwika.


Mudzawazindikira ndi zipatso zao. Kodi atchera mphesa paminga, kapena nkhuyu pamtula?


Pakuti mtengo uliwonse uzindikirika ndi chipatso chake. Pakuti anthu samatchera nkhuyu paminga, kapena pamtungwi samatchera mphesa.


Ndipo tsopano ndinena ndi inu, Lekani anthu amenewa, nimuwalole akhale; pakuti ngati uphungu umene kapena ntchito iyi ichokera kwa anthu, idzapasuka;


Kodi mkuyu ukhoza kubala azitona, abale anga, kapena mpesa kubala nkhuyu? Kotero madzi amchere sangathe kutulutsa okoma.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa