Mateyu 7:1 - Buku Lopatulika1 Musaweruze, kuti mungaweruzidwe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Musaweruze, kuti mungaweruzidwe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 “Musamaweruza anthu ena kuti ndi olakwa, kuwopa kuti Mulungu angakuweruzeni. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 “Musaweruze ena, kuti inunso mungadzaweruzidwe. Onani mutuwo |