Mateyu 6:8 - Buku Lopatulika8 Chifukwa chake inu musafanane nao: pakuti Atate wanu adziwa zomwe muzisowa, inu musanayambe kupempha Iye. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Chifukwa chake inu musafanane nao: pakuti Atate wanu adziwa zomwe muzisowa, inu musanayambe kupempha Iye. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 Inu musamatero ai, pakuti Atate anu amadziŵa zimene mukusoŵa, inu musanapemphe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Musakhale ngati iwo chifukwa Atate anu amadziwa zimene musowa musanapemphe. Onani mutuwo |