Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Mateyu 6:8 - Buku Lopatulika

8 Chifukwa chake inu musafanane nao: pakuti Atate wanu adziwa zomwe muzisowa, inu musanayambe kupempha Iye.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 Chifukwa chake inu musafanane nao: pakuti Atate wanu adziwa zomwe muzisowa, inu musanayambe kupempha Iye.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 Inu musamatero ai, pakuti Atate anu amadziŵa zimene mukusoŵa, inu musanapemphe.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Musakhale ngati iwo chifukwa Atate anu amadziwa zimene musowa musanapemphe.

Onani mutuwo Koperani




Mateyu 6:8
6 Mawu Ofanana  

Ambuye, chikhumbo changa chonse chili pamaso panu; ndipo kubuula kwanga sikubisika kwa Inu.


Pakuti anthu akunja azifunitsa zonse zimenezo; pakuti Atate wanu wa Kumwamba adziwa kuti musowa zonse zimenezo.


Pakuti izi zonse mitundu ya anthu a padziko lapansi amazifunafuna; koma Atate wanu adziwa kuti musowa zimenezi.


Musadere nkhawa konse; komatu m'zonse ndi pemphero, ndi pembedzero, pamodzi ndi chiyamiko, zopempha zanu zidziwike kwa Mulungu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa